Masalimo 18:41 - Buku Lopatulika41 Anafuula, koma panalibe wopulumutsa; ngakhale kwa Yehova, koma sanawavomereze. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Anafuula, koma panalibe wopulumutsa; ngakhale kwa Yehova, koma sanawavomereze. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Adakuwa kuti ena aŵathandize, koma panalibe woŵapulumutsa. Adalirira Chauta, koma sadaŵayankhe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa. Analirira kwa Yehova koma sanawayankhe. Onani mutuwo |