Masalimo 18:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo adani anga mwawalozetsa m'mbuyo kwa ine, kuti ndipasule ondidawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo adani anga mwawalozetsa m'mbuyo kwa ine, kuti ndipasule ondidawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Inu mudapirikitsa adani anga kuti andithaŵe, amene ankadana nane ndidaŵaononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Inu munachititsa adani anga kutembenuka, kuonetsa misana yawo pothawa, ndipo ine ndinawononga adani angawo. Onani mutuwo |