Masalimo 18:25 - Buku Lopatulika25 Pa wachifundo mukhala wachifundo; pa munthu wangwiro mukhala wangwiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pa wachifundo mukhala wachifundo; pa munthu wangwiro mukhala wangwiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Kwa anthu okhulupirika, Inu Mulungu mumadziwonetsa okhulupirika. Kwa anthu aungwiro, mumadziwonetsa abwino kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu; kwa anthu amakhalidwe abwino, Inu mumaonetsanso makhalidwe abwino, Onani mutuwo |