Masalimo 18:26 - Buku Lopatulika26 Pa woyera mtima mukhala woyera mtima; pa wotsutsatsutsa mukhala wotsutsana naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pa woyera mtima mukhala woyera mtima; pa wotsutsatsutsa mukhala wotsutsana naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Kwa anthu oyera mtima mumadziwonetsa okoma mtima, koma kwa anthu oipa mtima, mumawonetsa kunyansidwa nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu, koma kwa achinyengo mumaonetsanso kunyansidwa nawo. Onani mutuwo |