Masalimo 18:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti ndasunga njira za Yehova, ndipo sindinachitire choipa kusiyana ndi Mulungu wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti ndasunga njira za Yehova, ndipo sindinachitira choipa kusiyana ndi Mulungu wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ine ndidatsata njira za Chauta, sindidachite zoipa ndi kumsiya Mulungu wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pakuti ine ndinatsata njira za Yehova; ndilibe mlandu wochoka pamaso Mulungu wanga. Onani mutuwo |