Masalimo 18:20 - Buku Lopatulika20 Yehova anandibwezera monga mwa chilungamo changa; anandisudzula monga mwa kusisira kwa manja anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Yehova anandibwezera monga mwa chilungamo changa; anandisudzula monga mwa kusisira kwa manja anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Chauta adandipatsa mphotho molingana ndi ntchito zanga zabwino, adandifupa molingana ndi ungwiro wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa; molingana ndi makhalidwe anga abwino, Iye wandipulumutsa. Onani mutuwo |