Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 18:18 - Buku Lopatulika

18 Anandipeza ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Anandipeza ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adaniwo adandithira nkhondo pamene ndinali m'mavuto, koma Chauta adandichirikiza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto, koma Yehova anali thandizo langa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 18:18
12 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide analankhula kwa Yehova mau a nyimbo iyi tsikuli Yehova anampulumutsa m'dzanja la adani ake onse, ndi m'dzanja la Saulo.


Anandifikira ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga.


Ichi ndinali nacho, popeza ndinasunga malangizo anu.


Ndingakhale ndiyenda pakati pa nsautso, mudzandipatsa moyo; mudzatambasula dzanja lanu pa mkwiyo wa adani anu, ndipo dzanja lanu lamanja lidzandipulumutsa.


Yehova wa makamu ali ndi ife, Mulungu wa Yakobo ndiye pamsanje pathu.


Koma ine, ndidzaimbira mphamvu yanu; inde ndidzaimbitsa chifundo chanu mamawa, pakuti Inu mwakhala msanje wanga, ndi pothawirapo ine tsiku la nsautso yanga.


Ndidzamwazamwaza iwo monga ndi mphepo ya kum'mawa pamaso pa adani; ndidzayang'anira pamsana pao, si nkhope yao, tsiku la Tsoka lao.


Ndipo ndikwiya nao amitundu okhala osatekeseka ndi mkwiyo waukulu; pakuti ndinakwiya pang'ono, ndipo anathandizira choipa.


Kubwezera chilango nkwanga, kubwezera komwe, pa nyengo ya kuterereka phazi lao; pakuti tsiku la tsoka lao layandika, ndi zinthu zowakonzeratu zifulumira kudza.


Ndipo Davide anadololoka kwambiri, pakuti anthu ananena za kumponya iye miyala, pakuti mtima wao wa anthu onse unali ndi chisoni, yense chifukwa cha ana ake aamuna ndi aakazi. Koma Davide anadzilimbikitsa mwa Yehova Mulungu wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa