Masalimo 18:18 - Buku Lopatulika18 Anandipeza ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Anandipeza ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Adaniwo adandithira nkhondo pamene ndinali m'mavuto, koma Chauta adandichirikiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto, koma Yehova anali thandizo langa. Onani mutuwo |