Masalimo 18:17 - Buku Lopatulika17 Anandipulumutsa ine kwa mdani wanga wamphamvu, ndi kwa iwo ondida ine, pakuti anandiposa mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Anandipulumutsa ine kwa mdani wanga wamphamvu, ndi kwa iwo ondida ine, pakuti anandiposa mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Adandipulumutsa kwa adani anga amphamvu, kwa onse amene ankadana nane, pakuti iwo anali amphamvu kwambiri kupambana ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, adani anga, amene anali amphamvu kuposa ine. Onani mutuwo |