Masalimo 18:12 - Buku Lopatulika12 Mwa kuchezemira kunali pamaso pake makongwa anakanganuka, matalala ndi makala amoto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mwa kuchezemira kunali pamaso pake makongwa anakanganuka, matalala ndi makala amoto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 M'kuŵala kumene kunali pamaso pake, munkafumira matalala ndi makala amoto, amene adabzola mitambo yophimba ija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera matalala, makala amoto ndi ziphaliwali zongʼanima. Onani mutuwo |