Masalimo 17:9 - Buku Lopatulika9 kundilanditsa kwa oipa amene andipasula, adani a pa moyo wanga amene andizinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 kundilanditsa kwa oipa amene andipasula, adani a pa moyo wanga amene andizinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 kuti asandiwone anthu oipa ofuna kupasula, ndiye kuti adani anga oopsaŵa amene akundizinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine, kuchoka kwa anthu amene ndi adani anga, amene andizungulira ine. Onani mutuwo |