Masalimo 17:8 - Buku Lopatulika8 Ndisungeni monga kamwana ka m'diso, ndifungatireni mu mthunzi wa mapiko anu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndisungeni monga kamwana ka m'diso, ndifungatireni mu mthunzi wa mapiko anu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mundisunge ngati mwana wa diso, munditeteze pansi pa mapiko anu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mundisunge ine ngati mwanadiso; mundibise mu mthunzi wa mapiko anu, Onani mutuwo |