Masalimo 17:4 - Buku Lopatulika4 Za machitidwe a anthu, ndachenjera ndi mau a milomo yanu ndingalowe njira za woononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Za machitidwe a anthu, ndachenjera ndi mau a milomo yanu ndingalowe njira za woononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kunena za ntchito za anthu, ine posunga mau anu, sindidatsate za anthu andeu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kunena za ntchito za anthu, monga mwa mawu a pakamwa panu, Ine ndadzisunga ndekha posatsata njira zachiwawa. Onani mutuwo |