Masalimo 17:3 - Buku Lopatulika3 Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku; mwandisuntha, simupeza kanthu; mwatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku; mwandisuntha, simupeza kanthu; mwatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ngakhale muyese mtima wanga, kapena kundipenyetsetsa usiku, kaya mundiyang'anitsitse chotani, mudzapeza kuti ndilibe mlandu. Pakamwa panga sipalankhula zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku, ngakhale mutandiyesa, simudzapeza kanthu; Ine ndatsimikiza kuti pakamwa panga sipadzachimwa. Onani mutuwo |