Masalimo 17:2 - Buku Lopatulika2 Pankhope panu patuluke chiweruzo changa; maso anu apenyerere zolunjika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pankhope panu patuluke chiweruzo changa; maso anu apenyerere zolunjika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kusalakwa kwanga kuwonekere poyera pa chiweruzo chanu, maso anu aone kulungama kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu; maso anu aone chimene ndi cholungama. Onani mutuwo |