Masalimo 17:13 - Buku Lopatulika13 Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ukani Yehova, Mumtsekereze, mumgwetse, landitsani moyo wanga kwa woipa ndi lupanga lanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Dzambatukani, Inu Chauta, mukumane nawo ndi kuŵagonjetsa. Mundipulumutse ndi lupanga lanu kwa anthu oipawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi; landitseni kuchoka kwa oyipa ndi lupanga lanu. Onani mutuwo |