Masalimo 17:12 - Buku Lopatulika12 Afanana ndi mkango wofuna kumwetula, ndi msona wa mkango wakukhala mobisalamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Afanana ndi mkango wofuna kumwetula, ndi msona wa mkango wakukhala mobisalamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ali ngati mkango wofunitsitsa kuti ukadzule, ngati chilombo cholusa cholalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iwo ali ngati mkango wofuna nyama; ngati mkango waukulu wokhala mobisala. Onani mutuwo |