Masalimo 17:11 - Buku Lopatulika11 Tsopano anatizinga m'mayendedwe athu, apenyetsetsa m'maso kuti atigwetse pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Tsopano anatizinga m'mayendedwe athu, apenyetsetsa m'maso kuti atigwetse pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Amangondilondola ndi kundizinga. Amandiyang'ana kuti apeze njira yondigwetsera pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Andisaka, tsopano andizungulira ndi maso awo atcheru, kuti andigwetse pansi. Onani mutuwo |