Masalimo 16:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti simudzasiya moyo wanga kumanda; simudzalola wokondedwa wanu avunde. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti simudzasiya moyo wanga kumanda; simudzalola wokondedwa wanu avunde. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 chifukwa simudzandisiya ku malo a anthu akufa, simudzalola kuti wokondedwa wanune ndikaole kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. Onani mutuwo |