Masalimo 15:4 - Buku Lopatulika4 M'maso mwake munthu woonongeka anyozeka; koma awachitira ulemu akuopa Yehova. Atalumbira kwa tsoka lake, sasintha ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 M'maso mwake munthu woonongeka anyozeka; koma awachitira ulemu akuopa Yehova. Atalumbira kwa tsoka lake, sasintha ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndi amene amanyoza munthu womkana Mulungu, koma amalemekeza anthu omvera Chauta. Ndi amene amachitadi zimene walonjeza, ngakhale zikhale zoŵaŵa chotani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa. Koma amalemekeza amene amaopa Yehova, amene amakwaniritsa zomwe walonjeza ngakhale pamene zikumupweteka, Onani mutuwo |