Masalimo 15:2 - Buku Lopatulika2 Iye wakuyendayo mokwanira, nachita chilungamo, nanena zoonadi mumtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Iye wakuyendayo mokwanira, nachita chilungamo, nanena zoonadi mumtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndi munthu amene amayenda mosalakwa, amene amachita zolungama nthaŵi zonse, amene amalankhula zinthu ndi mtima woona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Munthu wa makhalidwe abwino, amene amachita zolungama, woyankhula choonadi chochokera mu mtima mwake, Onani mutuwo |