Masalimo 15:1 - Buku Lopatulika1 Yehova, ndani adzagonera m'chihema mwanu? Adzagonera ndani m'phiri lanu lopatulika? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova, ndani adzagonera m'chihema mwanu? Adzagonera ndani m'phiri lanu lopatulika? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta, kodi ndani angathe kukhala m'Nyumba mwanu? Ndani angathe kukhala pa phiri lanu loyera? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika? Kodi ndani angathe kukhala mʼphiri lanu loyera? Onani mutuwo |