Masalimo 149:6 - Buku Lopatulika6 Nyimbo zakukweza Mulungu zikhale pakamwa pao, ndi lupanga lakuthwa konsekonse m'dzanja lao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Nyimbo zakukweza Mulungu zikhale pakamwa pao, ndi lupanga lakuthwa konsekonse m'dzanja lao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Atamande Mulungu kwambiri mokweza mau, malupanga akuthwa konsekonse ali m'manja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Matamando a Mulungu akhale pakamwa pawo, ndi lupanga lakuthwa konsekonse mʼmanja mwawo, Onani mutuwo |