Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 145:9 - Buku Lopatulika

9 Yehova achitira chokoma onse; ndi nsoni zokoma zake zigwera ntchito zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Yehova achitira chokoma onse; ndi nsoni zokoma zake zigwera ntchito zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Chauta ndi wabwino kwa onse, amachitira chifundo zamoyo zonse zimene adazilenga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova ndi wabwino kwa onse; amachitira chifundo zonse zimene anazipanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 145:9
12 Mawu Ofanana  

ndi zamoyo zonse zili pamodzi ndi inu, zouluka, ng'ombe, ndi zinyama zonse za dziko lapansi, pamodzi ndi inu; zonse zotuluka m'chingalawa, zinyama zonse za dziko lapansi.


Pakuti Yehova ndiye wabwino; chifundo chake chimanka muyaya; ndi chikhulupiriko chake ku mibadwomibadwo.


Izi zonse zikulindirirani, muzipatse chakudya chao pa nyengo yake.


Yehova ndiye wabwino ndi wolunjika mtima, chifukwa chake adzaphunzitsa olakwa za njira.


Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu.


ndipo sindiyenera Ine kodi kuchitira chifundo Ninive mzinda waukulu uwu; m'mene muli anthu oposa zikwi zana limodzi mphambu zikwi makumi awiri osadziwa kusiyanitsa pakati padzanja lao lamanja ndi lamanzere, ndi zoweta zambiri zomwe?


Yehova ali wabwino, ndiye polimbikirapo tsiku la msauko; ndipo adziwa iwo omkhulupirira Iye.


kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Koma sanadzisiyire Iye mwini wopanda umboni, popeza anachita zabwino, nakupatsani inu zochokera kumwamba mvula ndi nyengo za zipatso, ndi kudzaza mitima yanu ndi chakudya ndi chikondwero.


satumikiridwa ndi manja a anthu, monga wosowa kanthu, popeza Iye mwini apatsa zonse moyo ndi mpweya ndi zinthu zonse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa