Masalimo 145:8 - Buku Lopatulika8 Yehova ndiye wachisomo, ndi wachifundo; osakwiya msanga, ndi wa chifundo chachikulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yehova ndiye wachisomo, ndi wachifundo; osakwiya msanga, ndi wa chifundo chachikulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta ndi wokoma mtima ndi wachifundo, wosakwiya msanga, wodzaza ndi chikondi chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo, wosakwiya msanga ndi wodzaza ndi chikondi chosasinthika. Onani mutuwo |