Masalimo 145:7 - Buku Lopatulika7 Adzabukitsa chikumbukiro cha ubwino wanu waukulu, nadzaimbira chilungamo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Adzabukitsa chikumbukiro cha ubwino wanu waukulu, nadzaimbira chilungamo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adzasimba za ubwino wanu, adzaimba nyimbo zotamanda kulungama kwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Adzakondwerera kuchuluka kwa ubwino wanu, ndi kuyimba mwachimwemwe za chilungamo chanu. Onani mutuwo |