Masalimo 145:4 - Buku Lopatulika4 Mbadwo wina udzalemekezera ntchito zanu mbadwo unzake, ndipo udzalalikira zamphamvu zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mbadwo wina udzalemekezera ntchito zanu mbadwo unzake, ndipo udzalalikira zamphamvu zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mibadwo ndi mibadwo idzatamanda ntchito zanu, idzalalika ntchito zanu zamphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mʼbado wina udzayamikira ntchito yanu kwa mʼbado wina; Iwo adzafotokoza za machitidwe anu amphamvu. Onani mutuwo |