Masalimo 145:5 - Buku Lopatulika5 Ndidzalingalira ulemerero waukulu wa ulemu wanu, ndi ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndidzalingalira ulemerero waukulu wa ulemu wanu, ndi ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidzasinkhasinkha za ulemerero ndi za ufumu wanu waukulu, ndidzalingalira za ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Adzayankhula ulemerero wokongola waufumu wanu, ndipo ine ndidzalingalira za ntchito zanu zodabwitsa. Onani mutuwo |