Masalimo 145:2 - Buku Lopatulika2 Masiku onse ndidzakuyamikani; ndi kulemekeza dzina lanu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Masiku onse ndidzakuyamikani; ndi kulemekeza dzina lanu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzakuthokozani tsiku ndi tsiku, ndidzatamanda dzina lanu mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzakutamandani tsiku ndi tsiku ndi kulemekeza dzina lanu ku nthawi za nthawi. Onani mutuwo |