Masalimo 145:1 - Buku Lopatulika1 Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu; ndipo ndidzalemekeza dzina lanu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu; ndipo ndidzalemekeza dzina lanu kunthawi za nthawi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndidzakuyamikani, Inu Mulungu wanga, mfumu yanga, ndidzalemekeza dzina lanu nthaŵi zonse mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu yanga; ndidzatamanda dzina lanu ku nthawi za nthawi. Onani mutuwo |