Masalimo 144:9 - Buku Lopatulika9 Ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano, Mulungu; pa chisakasa cha zingwe khumi ndidzaimbira zakukulemekezani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano, Mulungu; pa chisakasa cha zingwe khumi ndidzaimbira zakukulemekezani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano, Inu Mulungu. Ndidzakuimbirani zeze wa nsambo khumi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu; ndidzakuyimbirani nyimbo pa zeze wa nsambo khumi, Onani mutuwo |