Masalimo 144:8 - Buku Lopatulika8 amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 amene amalankhula zabodza, ndipo amalumbira zonama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo. Onani mutuwo |