Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 144:8 - Buku Lopatulika

8 amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 amene amalankhula zabodza, ndipo amalumbira zonama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 144:8
13 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anati kwa mfumu ya Sodomu, Dzanja langa ndamtukulira Yehova, Mulungu Wamkulukulu, mlengi wa kumwamba ndi dziko lapansi


M'kamwa mwake mwadzala kutemberera ndi manyengo ndi kuchenjerera; pansi pa lilime lake pali chivutitso chopanda pake.


Potero anawasamulira dzanja lake, kuti awagwetse m'chipululu:


Amanena za bodza munthu yense ndi mnansi wake, amanena ndi mlomo wothyasika, ndi mitima iwiri.


Ndipo akadza kundiona wina angonena bodza; mumtima mwake adzisonkhera zopanda pake, akanka nayenda namakanena.


Oipa achita chilendo chibadwire, asokera kuyambira kubadwa kwao, nanena bodza.


Komatu amkhalira upo kuti amkankhire pansi ulemu wake; akondwera nao mabodza; adalitsa ndi m'kamwa mwao, koma atemberera mumtima.


Iye adya phulusa; mtima wodzinyenga wampambutsa, kuti iye sangapulumutse moyo wake, pena kunena, Kodi simuli kunama m'dzanja langa lamanja?


Ndipo ngati dzanja lako lamanja likulakwitsa iwe, ulidule, nulitaye; pakuti nkwabwino kwa iwe kuti chimodzi cha ziwalo zako chionongeke, losamuka thupi lako lonse ku Gehena.


Pakuti ndikweza dzanja langa kuloza kumwamba, ndipo nditi, Pali moyo wanga kosatha,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa