Masalimo 143:9 - Buku Lopatulika9 Mundilanditse kwa adani anga, Yehova; ndibisala mwa Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mundilanditse kwa adani anga, Yehova; ndibisala mwa Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Inu Chauta, pulumutseni kwa adani anga, chifukwa ndathaŵira kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova, pakuti ndimabisala mwa Inu. Onani mutuwo |