Masalimo 139:5 - Buku Lopatulika5 Munandizinga kumbuyo ndi kumaso, nimunaika dzanja lanu pa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Munandizinga kumbuyo ndi kumaso, nimunaika dzanja lanu pa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo, ndipo mumandisanjika dzanja lanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo komwe; mwasanjika dzanja lanu pa ine. Onani mutuwo |