Masalimo 139:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo ndikati, Koma mdima undiphimbe, ndi kuunika kondizinga kukhale usiku. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo ndikati, Koma mdima undiphimbe, ndi kuunika kondizinga kukhale usiku. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndikanena kuti, “Mdima undiphimbe, kuŵala kumene kwandizinga kusanduke mdima,” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndikanena kuti, “Zoonadi, mdima udzandibisa ndithu ndipo kuwunika kukhale mdima mondizungulira,” Onani mutuwo |