Masalimo 137:1 - Buku Lopatulika1 Ku mitsinje ya ku Babiloni, kumeneko tinakhala pansi, inde tinalira, pokumbukira Ziyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ku mitsinje ya ku Babiloni, kumeneko tinakhala pansi, inde tinalira, pokumbukira Ziyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 M'mbali mwa mitsinje ya ku Babiloni, kumeneko tidakhala pansi nkumalira tikukumbukira Ziyoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira pamene tinakumbukira Ziyoni. Onani mutuwo |