Masalimo 136:26 - Buku Lopatulika26 Yamikani Mulungu wa Kumwamba, pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Yamikani Mulungu wa kumwamba; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Thokozani Mulungu wakumwamba, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Yamikani Mulungu wakumwamba, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |