Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 136:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anawapha mafumu omveka; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anawapha mafumu omveka; pakuti chifundo chake nchosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adaphanso mafumu otchuka, pakuti chikondi chake nchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Napha mafumu amphamvu, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 136:18
1 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene munafika pamalo pano, Sihoni mfumu ya Hesiboni, ndi Ogi mfumu ya Basani, anatuluka kudzakomana nafe kunkhondo, ndipo tinawakantha;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa