Masalimo 132:18 - Buku Lopatulika18 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Adani ake ndidzaŵaveka manyazi ngati nsalu, koma iye yekhayo adzavala chisoti choŵala chachifumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ndidzaveka adani ake manyazi, koma chipewa chaufumu pamutu pake chidzakhala chowala.” Onani mutuwo |