Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 132:18 - Buku Lopatulika

18 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adani ake ndidzaŵaveka manyazi ngati nsalu, koma iye yekhayo adzavala chisoti choŵala chachifumu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndidzaveka adani ake manyazi, koma chipewa chaufumu pamutu pake chidzakhala chowala.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 132:18
14 Mawu Ofanana  

Iwo akudana nawe adzavala manyazi; ndi hema wa oipa adzakhala kuli zii.


Limkhalire ngati chovala adzikuta nacho, ndi lamba limene adzimangirira nalo m'chuuno chimangirire.


Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Achite manyazi, nadodome iwo akukondwera chifukwa cha choipa chidandigwera. Avekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.


Munthu amatamandidwa monga mwa nzeru yake; koma wokhota mtima adzanyozedwa.


Ndipo ambiri a iwo ogona m'fumbi lapansi adzauka, ena kunka kumoyo wosatha, ndi ena kumanyazi ndi mnyozo wosatha.


Ndipo Yesu anadza nalankhula nao, nanena, Mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine Kumwamba ndi padziko lapansi.


Ndipo mngelo wachisanu ndi chiwiri anaomba lipenga, ndipo panakhala mau aakulu mu Mwamba, ndi kunena, Ufumu wa dziko lapansi wayamba kukhala wa Ambuye wathu, ndi wa Khristu wake: ndipo adzachita ufumu kufikira nthawi za nthawi.


Iwo adzachita nkhondo pa Mwanawankhosa, ndipo Mwanawankhosa adzawagonjetsa, chifukwa ali Mbuye wa ambuye, ndi Mfumu ya mafumu; ndipo adzawalakanso iwo akukhala naye, oitanidwa, ndi osankhika ndi okhulupirika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa