Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 132:17 - Buku Lopatulika

17 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga; ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga; ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 “Davide ndidzammeretsera chiphukira kumeneko. Ndamkonzera nyale wodzozedwa wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 “Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide ndi kuyikapo nyale ya wodzozedwa wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 132:17
11 Mawu Ofanana  

Ndipo ndidzamninkha mwana wake fuko limodzi, kuti Davide mtumiki wanga akhale chikhalire ndi nyali pamaso panga mu Yerusalemu, mzinda umene ndinadzisankhira kuikapo dzina langa.


Koma chifukwa cha Davideyo Yehova Mulungu wake anampatsa nyali mu Yerusalemu, kumuikira mwana wake pambuyo pake, ndi kukhazikitsa Yerusalemu;


Koma Yehova sanafune kuononga Yuda, chifukwa cha Davide mtumiki wake monga adamuuza, kuti adzampatsa nyali ya kwa ana ake kosalekeza.


Koma Yehova sanafune kuononga nyumba ya Davide chifukwa cha pangano adalichita ndi Davide, ndi monga adalonjeza kumpatsa iye ndi ana ake nyali nthawi zonse.


Ndipo anakweza nyanga ya anthu ake, chilemekezo cha okondedwa ake onse; ndiwo ana a Israele, anthu a pafupi pa Iye. Aleluya.


Ndipo ndidzaika dzanja lake panyanja, ndi dzanja lamanja lake pamitsinje.


Koma munakweza nyanga yanga ngati ya njati; anandidzoza mafuta atsopano.


Tsiku ilo ndidzameretsera nyumba ya Israele nyanga; ndipo ndidzakutsegulira pakamwa pakati pao; motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.


Ndipo Iye anatikwezera ife nyanga ya chipulumutso, mwa fuko la Davide mwana wake.


Otsutsana ndi Yehova adzaphwanyika; kumwamba Iye adzagunda pa iwo; Yehova adzaweruza malekezero a dziko. Ndipo adzapatsa mphamvu mfumu yake, nadzakweza nyanga ya wodzozedwa wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa