Masalimo 132:17 - Buku Lopatulika17 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga; ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga; ndakonzeratu wodzozedwa wanga nyali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Davide ndidzammeretsera chiphukira kumeneko. Ndamkonzera nyale wodzozedwa wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide ndi kuyikapo nyale ya wodzozedwa wanga. Onani mutuwo |