Masalimo 130:4 - Buku Lopatulika4 Koma kwa Inu kuli chikhululukiro, kuti akuopeni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Koma kwa Inu kuli chikhululukiro, kuti akuopeni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma inu mumakhululukira, nchifukwa chake timakulemekezani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma kwa Inu kuli chikhululukiro; nʼchifukwa chake mumaopedwa. Onani mutuwo |