Masalimo 130:5 - Buku Lopatulika5 Ndilindira Yehova, moyo wanga ulindira, ndiyembekeza mau ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndilindira Yehova, moyo wanga ulindira, ndiyembekeza mau ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndimayembekeza chithandizo cha Chauta, ndimayembekeza ndi mtima wonse, ndipo ndimakhulupirira mau ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera, ndipo ndimakhulupirira mawu ake. Onani mutuwo |