Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 130:5 - Buku Lopatulika

5 Ndilindira Yehova, moyo wanga ulindira, ndiyembekeza mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndilindira Yehova, moyo wanga ulindira, ndiyembekeza mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndimayembekeza chithandizo cha Chauta, ndimayembekeza ndi mtima wonse, ndipo ndimakhulupirira mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera, ndipo ndimakhulupirira mawu ake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 130:5
17 Mawu Ofanana  

Ndadikira chipulumutso chanu, Yehova.


Inu ndinu pobisalapo panga, ndi chikopa changa; ndiyembekezera mau anu.


Kuti ndikhale nao mau akuyankha wonditonza; popeza ndikhulupirira mau anu.


Kumbukirani mau a kwa mtumiki wanu, amene munandiyembekezetsa nao.


Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.


Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu.


Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova.


Moyo wathu walindira Yehova; Iye ndiye thandizo lathu ndi chikopa chathu.


Kuyembekeza ndayembekeza Yehova; ndipo anandilola, namva kufuula kwanga.


Moyo wanga ukhalira chete Mulungu yekha; chipulumutso changa chifuma kwa Iye.


Moyo wanga, ukhalire chete Mulungu yekha; pakuti chiyembekezo changa chifuma kwa Iye.


Inde m'njira ya maweruziro anu, Yehova, ife talindira Inu; moyo wathu ukhumba dzina lanu, ndi chikumbukiro chanu.


Chifukwa chake Yehova adzadikira, kuti akukomereni mtima, ndipo chifukwa chake Iye adzakuzidwa, kuti akuchitireni inu chifundo; pakuti Yehova ndiye Mulungu wa chiweruziro; odala ali onse amene amdikira Iye.


Ndipo ndidzalindira Yehova, amene wabisira a nyumba ya Yakobo nkhope yake, ndipo ndidzamyembekeza Iye.


Ndipo onani, mu Yerusalemu munali munthu, dzina lake Simeoni; ndipo munthu uyu, wolungama mtima ndi wopemphera, analikulindira matonthozedwe a Israele; ndipo Mzimu Woyera anali pa iye.


Ndipo iye anafikako pa nthawi yomweyo, navomerezanso kutama Mulungu, nalankhula za Iye kwa anthu onse akuyembekeza chiombolo cha Yerusalemu.


kuti mwa zinthu ziwiri zosasinthika, m'mene Mulungu sangathe kunama, tikakhale nacho chotichenjeza cholimba, ife amene tidathawira kuchigwira chiyembekezo choikika pamaso pathu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa