Masalimo 130:2 - Buku Lopatulika2 Ambuye, imvani liu langa; makutu anu akhale chimverere mau a kupemba kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ambuye, imvani liu langa; makutu anu akhale chimverere mau a kupemba kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ambuye imvani liwu langa. Tcherani khutu kuti mumve kupemba kwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ambuye imvani mawu anga. Makutu anu akhale tcheru kumva kupempha chifundo kwanga. Onani mutuwo |