Masalimo 12:2 - Buku Lopatulika2 Amanena za bodza munthu yense ndi mnansi wake, amanena ndi mlomo wothyasika, ndi mitima iwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Amanena za bodza munthu yense ndi mnansi wake, amanena ndi mlomo wothyasika, ndi mitima iwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Aliyense amangonamiza mnzake, amathyasika ndi pakamwa pake, amalankhula ndi mitima iŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Aliyense amanamiza mʼbale wake; ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo. Onani mutuwo |