Masalimo 119:2 - Buku Lopatulika2 Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ngodala amene amasunga malamulo a Chauta, amene amafunafuna Chauta ndi mtima wao wonse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Odala ndi amene amasunga malamulo ake, amene amafunafuna Iyeyo ndi mtima wawo wonse. Onani mutuwo |