Masalimo 119:141 - Buku Lopatulika141 Wamng'ono ine, ndi wopepulidwa; koma sindiiwala malemba anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014141 Wamng'ono ine, ndi wopepulidwa; koma sindiiwala malemba anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa141 Ine ndine wamng'ono ndi wonyozeka, komabe sindiiŵala malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero141 Ngakhale ndili wamngʼono ndi wonyozeka, sindiyiwala malangizo anu. Onani mutuwo |