Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:140 - Buku Lopatulika

140 Mau anu ngoyera ndithu; ndi mtumiki wanu awakonda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

140 Mau anu ngoyera ndithu; ndi mtumiki wanu awakonda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

140 Malonjezo anu ndi otsimikizika, ndipo ine mtumiki wanu ndimaŵakonda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

140 Mawu anu ndi woyera kwambiri nʼchifukwa chake mtumiki wanune ndimawakonda.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:140
12 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ndiyesa ngolunjika malangizo anu onse akunena zonse; koma ndidana nazo njira zonse zonyenga.


Ndipo ndidzadzikondweretsa nao malamulo anu, amene ndiwakonda.


Mau a Yehova ndi mau oona; ngati siliva woyenga m'ng'anjo yadothi, yoiyeretsa kasanu ndi kawiri.


Mudzawasunga, Yehova, mudzawatchinjirizira mbadwo uno kunthawi zonse.


Mulungu ndiye wangwiro m'njira zake; mau a Yehova ngoyengeka; ndiye chikopa cha onse okhulupirira Iye.


Malangizo a Yehova ali olungama, akukondweretsa mtima; malamulo a Yehova ali oyera, akupenyetsa maso.


Mau onse a Mulungu ali oyengeka; ndiye chikopa cha iwo amene amkhulupirira.


Chotero chilamulo chili choyera, ndi chilangizo chake nchoyera, ndi cholungama, ndi chabwino.


Koma ngati ndichita chimene sindichifuna, ndivomerezana nacho chilamulo kuti chili chabwino.


Pakuti monga mwa munthu wa m'kati mwanga, ine ndikondwera ndi chilamulo cha Mulungu:


lirani monga makanda alero mkaka woyenera, wopanda chinyengo, kuti mukakule nao kufikira chipulumutso;


pakuti kale lonse chinenero sichinadze ndi chifuniro cha munthu; koma anthu a Mulungu, ogwidwa ndi Mzimu Woyera, analankhula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa