Masalimo 115:3 - Buku Lopatulika3 Koma Mulungu wathu ndiye ali m'mwamba; achita chilichonse chimkonda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma Mulungu wathu ndiye ali m'mwamba; achita chilichonse chimkonda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mulungu wathu ali kumwamba, amachita chilichonse chimene afuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu wathu ali kumwamba; Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa. Onani mutuwo |