Masalimo 113:9 - Buku Lopatulika9 Asungitsa nyumba mkazi wosaona mwana, akhale mai wokondwera ndi ana. Aleluya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Asungitsa nyumba mkazi wosaona mwana, akhale mai wokondwera ndi ana. Aleluya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amapatsa banja mkazi wosabala, namsandutsa mai wosangalala wa ana. Tamandani Chauta! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake monga mayi wa ana wosangalala. Tamandani Yehova. Onani mutuwo |