Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 113:7 - Buku Lopatulika

7 Amene autsa wosauka kumchotsa kufumbi, nakweza waumphawi kumchotsa kudzala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Amene autsa wosauka kumchotsa kufumbi, nakweza waumphawi kumchotsa kudzala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Amakweza munthu wosauka kuchokera ku fumbi, ndipo amatulutsa ku dzala anthu osoŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 113:7
20 Mawu Ofanana  

Popeza ndinakukuza iwe kuchokera kufumbi, ndi kukuika iwe mfumu ya anthu anga Israele, koma iwe unayenda m'njira ya Yerobowamu, ndi kuchimwitsa anthu anga Israele, kuputa mkwiyo wanga ndi machimo ao;


Ndipo anadzitengera phale, kudzikanda nalo; nakhala pansi m'maphulusa.


kuika opeputsidwa pamalo ponyamuka, kuti iwo a maliro akwezedwe kosatekeseka.


Koma aika waumphawi pamsanje posazunzika, nampatsa mabanja ngati gulu la nkhosa.


Mphamvu yanga yauma ngati phale; ndi lilime langa likangamira kunsaya zanga; ndipo mwandifikitsa kufumbi la imfa.


Akufa anu adzakhala ndi moyo; mitembo yao idzauka. Ukani muimbe, inu amene mukhala m'fumbi; chifukwa mame ako akunga mame a pamasamba, ndipo dziko lapansi lidzatulutsa mizimu.


Ndipo mitengo yonse yakuthengo idzadziwa kuti Ine Yehova ndatsitsa mtengo wosomphoka, ndakuza mtengo waung'ono, ndaumitsa mtengo wauwisi, ndi kuphukitsa mtengo wouma; Ine Yehova ndanena ndi kuchichita.


Mverani, abale anga okondedwa; kodi Mulungu sanasankhe osauka a dziko lapansi akhale olemera ndi chikhulupiriro, ndi olowa nyumba a ufumu umene adaulonjeza kwa iwo akumkonda Iye?


Nanga mfumu ya Israele inatulukira yani; inu mulikupirikitsa yani? Galu wakufa, kapena nsabwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa