Masalimo 113:7 - Buku Lopatulika7 Amene autsa wosauka kumchotsa kufumbi, nakweza waumphawi kumchotsa kudzala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Amene autsa wosauka kumchotsa kufumbi, nakweza waumphawi kumchotsa kudzala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Amakweza munthu wosauka kuchokera ku fumbi, ndipo amatulutsa ku dzala anthu osoŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi ndi kutukula munthu wosowa kuchoka pa dzala; Onani mutuwo |