Masalimo 110:7 - Buku Lopatulika7 Adzamwa kumtsinje wa panjira; chifukwa chake adzaweramutsa mutu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Adzamwa kumtsinje wa panjira; chifukwa chake adzaweramutsa mutu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adzamwa mu mtsinje wam'njira, ndipo adzaŵeramutsa mutu monyadira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira; choncho adzaweramutsa mutu wake. Onani mutuwo |