Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 110:7 - Buku Lopatulika

7 Adzamwa kumtsinje wa panjira; chifukwa chake adzaweramutsa mutu wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Adzamwa kumtsinje wa panjira; chifukwa chake adzaweramutsa mutu wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Adzamwa mu mtsinje wam'njira, ndipo adzaŵeramutsa mutu monyadira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira; choncho adzaweramutsa mutu wake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 110:7
16 Mawu Ofanana  

Aone yekha chionongeko chake m'maso mwake, namwe mkwiyo wa Wamphamvuyonse.


Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi,


Ndipo tsopano mutu wanga udzakwezeka pamwamba pa adani anga akundizinga; ndipo ndidzapereka m'chihema mwake nsembe za kufuula mokondwera; ndidzaimba, inde, ndidzaimbira Yehova zomlemekeza.


Ndipo Inu Yehova, ndinu chikopa changa; ulemerero wanga, ndi wondiweramutsa mutu wanga.


Chifukwa chake Yehova wa makamu atero za aneneri: Taonani, ndidzadyetsa iwo chowawa, ndidzamwetsa iwo madzi andulu; pakuti kwa aneneri a ku Yerusalemu kuipitsa kwatulukira kunka ku dziko lonse.


Ndipo panali chaka cha makumi atatu ndi zisanu ndi ziwiri cha undende wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda, mwezi wakhumi ndi iwiri, tsiku la makumi awiri ndi asanu la mwezi, Evili-Merodaki mfumu ya ku Babiloni anaweramutsa mutu wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda, namtulutsa iye m'ndende;


Koma Yesu anayankha nati, Inu simudziwa chimene mupempha. Kodi mukhoza kumwera chikho nditi ndidzamwere Ine? Iwo ananena kwa Iye, Ife tikhoza.


Anamukanso kachiwiri, napemphera, nati, Atate wanga, ngati ichi sichingandipitirire, koma ndimwere ichi, kufuna kwanu kuchitidwe.


Kodi sanayenere Khristu kumva zowawa izi, ndi kulowa ulemerero wake?


Pamenepo Yesu anati kwa Petro, Longa lupanga m'chimake chake; chikho chimene Atate wandipatsa Ine sindimwere ichi kodi?


ndi kusanthula nthawi yiti, kapena nthawi yanji Mzimu wa Khristu wokhala mwa iwo analozera, pakuchitiratu umboni wa masautso a Khristu, ndi ulemerero wotsatana nao.


Pamenepo Mulungu anang'amba pokumbika paja pa Lehi, natulukamo madzi; namwa iye, nubwera moyo wake, natsitsimuka iye; chifukwa chake anawatcha dzina lake, Kasupe wa wofuula, ndiwo mu Lehi mpaka lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa